« How Mirza Insulted the Holy Prophet SAAW »






Bismillah Al-Rehman Al-Raheem

Anti Ahmadiyya Movement in Islam  

MMENE YEMWE ANAYAMBA GURU LA AHMADIYYA ANANYOZERA MTUMIKI MUHAMMAD (SAW)

OLEMBE    DR. SYED RASHID ALI.

 

Zonse zotamandidwa ndi za Allah, umodzi yekha ndipo ndiyemweyo. Chikondi chake ndi madalitso yangagwele mwamuya-ya-ya pa woyela Mtumiki Muhammad pambuyo pache palibe wina Mtumiki.

Anthu a kudziko ya Ulaya (Britain) anatenga mwaupandu ula-mililo wa a muslim wa India sub-contient ndipo lolemekezedwa linatumidwa kudziko la  India ku chokela ku nyumba ya malamulo la ku Ulaya kuti apeze njira yomwe angaletse chikhulupililo cha Jihadi.

 

Pambuyo pa zaka ziwiri zomafufuza, bungweri linapereka zofufuza zao  zomwe mutu wace unati “ Kufunika kuganizila kuti a musilamu abvomere mutsogoreri wao wa ci Islam pa  maso  pao. Lero maganiza  a zopeza munthu emwe a ngazipange ngati mtumiki wansembe. Mirza Ghulam Ahmad anasankhidwa kuti a kwaniritse nchito chi*****wa chakuti anali wa mbado wa anthu a ku Ulaya, ndiponso makharidwe ake ndi chikhulupiriro chace cha za  Mulungu.

 

Anapeza mwa iye munthu wocita zabwino. Patapita zaka, anabvomela mkalata yomwe analemba kwa olamurira wamkulu wa Punjab kuti anangozipanga ku khala ngati Mtumiki wansembe mau  awa apezeka mbukhu lache; kitab-ul-Bariyah. Roohani Khazain vol. 13 p.350 kwa aliyense kuti aone. Mirza Ghulam anakhula kapolo wa Islam, osinthitsa umoyo ndipo anakwela ndime zambiri ndi zomwe zinali kuchedwa Mtumiki. Zikhalidwe zake zinapangitsa kuti apite pamwamba pa mipingo yambiri. Kuyambira pa ukupolo wa Islam, wositha chikhulupililo cha Islam-M’mahadith-Mujaddid- Oringana ndi Eisa ibne Maryam (mueneri woronjezedwa)- Imam Mahdi-Mtumiki wotumidwa- Adam-Sari- Noah- Abraham- Isaac- Ishmael- Joseph- David- Solomon- Jonas- Lord Krishna- Jai Singh Bahadwi, palibe pomwe ankaimirira pothela pache, zikhulupiriro zace za bodza zinamukakamiza kunena kuti anali woyela Mtumiki Muhammad      ndoponso kubwera kwachiwiri. Ndipo analemba : “ Uyo amene asiyamika ine ndi Mustafa sanandione ndiponso  sanandizindikile.” (Roohani Khazain vol. P.259). Lero emwe anayamba ngati kapolo anakhala mfumu mwa iye yekha.

 

Mirza Ghulam Ahmad anakhazikisha guru la Ahmadiyya zaka zikwi-zikwi zapita kumbuyo uku poyendeletsedwa ndi a British kufikira lero lino. Angakhale lero anthu amene apezeka m’gururi aphatikiza aja omwe ali ndi mantha akubwelanso mu  chiIslam. Onse azindikila kuti ngati m’Muslim wachoka ndi kutsata Ahmadiyyah azachepetsa unyiji wa a Muslim. A Muslim amaphunzilo osiyana-siyana ndi a maganizo oasiyana- siyana m’maiko onse ndi ogwirizana muchikhulupiriro cao cha kuti Mirza Ghulam Ahmad anali ochimwa osakhulupirira ndipo sanali m’njira   yachiIslam, ndiponso aliyense omtsatira, angakhali kuti ndi Qadiani, Ahmadi wa ku Lahori, nayeso ndi wochoka mnjira ya chi Islam. Mu nkhani  ya kutha kwa caka ca 1974, ophunzira mwakuya pa za Mulungu analengeza kuti Mirza Ghulam Ahmad ndi onse omutsatira  alibe chikhuhipiriro cha Islam.

Angakhale lero, kuonetsa monga ali a Sunni Muslim ndipo kaswili wa Islam, guru la Ahmadiyyah ipitiriza kunama anthu osaphunzila ndi osanka omwe ali, a Muslim m’balu zosiyana- siyana za dziko. Zolemba zao ziimiliza mbali imodzi mwadala kuyopa zo khulupilira za omwe anayamba gululi.

 

Mwa tsopano apa, pepala linalembedwa ndi ku turutsidwa ndi guru la Ahmadiyyah/Qadianiyah mu mbari zambiri za m’maiko “Ahmad muchitamando  cha zikhalidwe za Indo-Pakistan, maina monga Ghulam Ahmad, Ghulam Rasool , Ghulam Ali Kapena Abdul Rahman ndi ena ndi maina opangidwa ndiponso yatanthauza Ghulam (Kapolo) wa Ahmad, Kapolo wa Rasool, Kapolo wa Ali kapena wanchito wa Rehman (wachifundo). Ndichodabwitsa ndiponso umene Ghulam Kapena Kapolo wa Ahmed alamurira mfumu yake ?

 

Mpepalari mupezeka nkhani zomwe zinalembedwa ndi yemwe anayamba gulu la Ahmadiyya, Mirza Ghulam Ahmad Qadiani, kuyesa kuonetsa kuti anali ledzela ndi chikundi cha woyela Mtumiki Muhammad (S.A.W), odzala ndi zithokoza za Allah, Qur’an loyela la Islam. Zomwe analemba Ghulam simuonetsa munthu wabwino. Koma yamwe Ahmad anali ndi madela awiri osiyana mu umoyo wace.

Dela loyamba linacokela ku umwana wace kufika koyambila kwa ukulu wa umoyo wake. Popeza kuti anabadwa mu banja la Muslim, pa nthawi anali wachikhulupiliro cha Sunni Muslim. Inali pa nthawi imene pomwe ananenelera mobwezara za chikulupiliro cha Sunni Muslim. Inali pa nthawi imeneyi pomwe ananenelera mobwezapo za chikhulipiliro cha Muslim Ahle-Sunnah wal Jammat, ndi chikondi ca woyela Mtumiki wa Islam ndi kufuna kwace kugwila nchito ya Islam. Angakhale kuti analandila maphunziko ache atsopano ku  sukulu    (madrassah) la maphunziko a Mulungu  kapena kuti anapeza ulangizi wa uzimu kulingana ndi mwanabo koma anali kuzithandiza yekha kupanga ziganizo ndi ndakatulo. Ngati kunali kucoka mnjira yokhazikitsidwa ya ahle Sunnah- Jamaat, ici sichinonekele.

 

Pambuyo pace, maganizo ndi zikhulupililo zace zinaonetsa kusintha ndipo anaonetsa kucotsa nzeru kuzomwe anali kunena ndi nthawi, anayambaso kucita zinthu zosayenera ndipo anaonetsa kucotsa nzeru kuzomwe anali kunena ndi kulemba sosaenela a Muslim. Koma kupita kwa nthawi, anayambaso kucita zinthu zosayenela. Ndipo iyi mbali yoipa ya Mirza Ghulam Ahmad inabisidwa ku anthu ndipo sinalembedwe m’mabukhu ya Guru la Ahmadiyya.

 

Mbali ina yomwe ifunika ku  kumbukira ndi zolemba za Mirza Ghulam Ahmad momwe anabvomela kuti anali kudwala matenda osiyana siyana ya mubongo yomwe anali ku  sokoneza maganizo ace . Akunena matenda monga a Machola, Minejaitisi, kuyiwala zinthu mwamsanga , khunyu, chizwezwe, kutaya madzi kawiri-kawiri. Anenanso matenda ena monga unyomwa ndi kusowa mphamvu ya kumvana. Akunena zamankhwala ambiri omwe ankazipangila ndipo ena omwe anali kutenga ku anthu. Akunenanso kumwa zinthu monga mu wine kukhala ngati mankhwara. Anali kulota angelo omwe anali kumuuza mtengo kapena mankhwala ambiri ya kuti amunthandize pakuonjeza mphamu za kumva wace. Ndipo tsiku lina Mulungu anamuuza kuturo kuti akonze mankhwala ya kumwa ndipo chimodzi chomwe chi nali kufunika kusakaniza mu mankhwala amenewa cinali OPIUM.

Kodi analidi odzala ndi chikundi cha Mtumiki oyela ? Kodi anali Mtumiki ? Kapena zinali nchito zace bongo wodwala chi*****wa ca kumwa OPIUM ndi mowa?

M’matsamba yokonkhapo, ndizaonetsa zolembedwa zopezeka m’mabukhu yolembedwa ndi Mirza Ghulam Ahmad kuti owelenga aganizile okha m’mene munthuyu anali. Chizakhala kuti imwe kupeza colinga ca emwe anapeza guru la Ahmadiyyah.

 

MIRZA GHULAM AHMAD NDI MULUNGU WACE

 

Mu zolembedwa zao a guru la Ahmadiyya azionetsa za cikondi ca mtsogeleri wao ndi chithokhozo cha Allah. Kulondora zilembedwe za m’mabukhu mwace zionetsa kuti Mirza Ghulam Ahmad WAHI ndizo khumba zinamulengetsa iye kutenga njira ina.

“ Ndinaona m’maso mwanga kuti ine ndine Mulungu ndikukhulugilira kuti umulungu unalowa mu thupi langa ndipo ndinali kunena kuti tifuna m’mwamba ndi pansi. Ndipo ndinalenga m’mwamba ndi pansi. (Roohani Khazain vol. 13 p.103).

Tsiku lina Hazrat Maseeh Mowood anaulula momwe anali kumvelera. Anaulula izi ci*****wa anali kuzimwera wamphamvu zomwe zalengezedwa ndi Mulungu.

( Trust N° 34, Islam Quarbani p.12 Qazi la Muhammad Qadiani, emwe anali mzace wa Mirza Ghulam).

 

(Subhan Allah! Kunama Allah pa za uwelewele ! Tipemphe Allah aticinjilize pa maganizo otayisa otele).

 

Mulungu Auza Mirza mu wahi wace

“ (Mirza !) Kumwamba ndi pansi kuli ndi iwe monga ku liri ndi ine. Ucokela kwa ine mchigwilizano ndi  kumva ine ndekha. Ucokela kwa ine monga ufumu wanga. Ucoka mwa ine monga mwana  wanga…ndimalakwa ndipo ndimacita zomwe nalengeza…Ndimaima kudwa. Tikupatsa ulemelero wa HAQ monga kuti Mulungu watsika kucoka kumwamba. Tikupatsa ulema wa mwana.”

(Haqiqat-ul-Wahy, Roohani Khazain vol. 22 p.79-99).

 

MIRZA GHULAM NDI MTUMIKI WOYELA MUHAMMAD

 

Mabukhu olembedwa ndi guru la Ahmadiyya ndilodzala ndi zolembedwa za Mirza zomwe zionetsa chikondi cha Mtumiki woyela Muhammad (Sal-Allaho alaihi wa Sallam). Kulondola zolembedwazi m’mabukuwa zionetsa nkhani yosiyana-siyana

Ghulam poyamba anali wa nchito wa AHMAD (MUHAMMAD) pambayo pace analedzela ndi chikondi cake. Kuledzela kumeneku kunaongonga umoyo wace ndipo anakhala Muhammad (SAW). Kodi amene amtsatila (Qadianis/ Ahmadis/ Lahoris/ Mirzais) adziwa  zolembedwazi ? Ngati ali oziziwa, kodi mnjira anazibisa kuti zitsadziwike?

 

Mirza Anena kuti ndi wa nchito (kapole) ndiponso ndi wa chikondi cha Mtumikiti woyela Muhammad SAW.

 

Zolembezedwa mu  kapepala komwe mutu wake ukuti, “Ahmadi athokoza Muhammad,” Mirza akunena kuti ndi wodzela ndi chikondi cha Muhammad (SAW).” Uyu odzicetsa yekha sali Mtumiki kapena otumidwa kupena kapolo olondola.”

(Man a Mirza Ghulam Ahmad, Akhbar Alhakum Qadian N° 23 vol. 5)

 

pambuyo pa Mulungu ndi oledzela ndi chikondi cha Muhammad. Ngati uyu simusilamu, Mulungu wanga ndine munthu usayenela.

(Zokambidwa za Mirza mpepala : “Ahmad nichithokozo wa Muhammad, p.1).

 

atanetsa omutsatila ake za chikondi wache cha Mtumiki woyela Muhammad (SAW), anapitiliza kuonetsa kuti, chikondi cake casandutsa thupi lake kukhala limodzi ndi thupi la Muhammad. Ndipo Mirza anati :

“ Allah anandipatsa udindo wa Mtumiki oyela ndipo anandipangitsa mtima kwa Mtumiki wacifundo wa kuti ine ndinakhala monga njira. Lero amene a tsata jamaat yanga akhala m’modzi wa sahaba ya juma yanga yomwe inali kuposa Mtumiki onse. Sichili chinthu chobisika kwa aja amene akwanitsa kuganiza kuti uku ndiko kutantha uza kwa mau asiyanitsa ine ndi Mustapha (Mtumiki woyela pbuh) akalibe kundiona ndipo sandidzindikila.

(Khutbah-e-Ilhamjah, Rohani Khazain, vol 16- pp.258-259)

 

kunali cabe kulindila nthawi ndipo anayamba kunena kuti anabadwa kutenga mulo a Mtumiki woyela( SAW). Lero GHULAM ANAKHALA  MFUMU.

Mirza Ghulam Anena kuti ndi Muhammad (SAW)

Mirza Ghulam akuti :

“Mtumiki woyela ali kubwela kawiri kapena tingati kuti kubwela koyumba kunatsimikidzidwa ndi kubwela kwa Messiah olengezedwa ndiponso Mahdi olengedzedwanso.”

(Roohan Khazain vol 17. p.249)

 

Mirza Ghulam anati :

“ Ndakhala ndikunena nthawi zambiri kuti kulingana ndi ndime (ya mu Qur’an oyela)”. Wa akhareena minhum lamma yalhayoo behim’as Buwoz, nditi Mtumikii m’modzi-modzi, Khatamul Ambiyyah ndipo zaka makumi awiri apitapo Mulungu anandipatsa dzina lakuti Mohammed ndi Ahmad mu Baraheen-e-Ahmadiyya ndi kupanga ine kukhala iye.

(Aik ghalti ka azala, Roohani Khazain vol 18 p.212).

 

Mirza Ghulam anati : “Mtumiki oyela anabadwa kawiri monga Mtumiki. Mkunena kwina tingati kuti chinalengedzedwa kuti Mtumiki woyela(SAW) adzakabadwanso mdziko ndiponso ichi chinatsimidzedwa ndi kubadwanso kwa Messiah olenjedzedwa ndiponso Mahdi.

(Tohfa-e-Golrwia, Roohani Khazain vo 17 p.249).

 

Mirza anati:

“ Pamene ndiri Mtumiki woyela obadwanso kwa chiwiri, ndipo zonse pomwe zinacitidwa ndi Muhammad kuonjezapo za utumiki, zioneka ngilasi kapena cilola changa, telo ndani wina emwe anganena kuti ndi Mtumiki mwa iye yekha ?”

(Ek Ghalti ka Izala, Roohani Khazain vol 18 p.212).

 

Zikhulupililo zotelezi ndi zilembedwe za Mirza Ghulam Ahmad zinapangitsa kuti omutsatira ace kuti anene mopanda manyazi zikhulupiliro zao.

Mirza Basheer Ahmad s/o Mirza Ghulam a kuti: Maseeh Mawood salephera kulota ku Mtumiki woyela (pbuh), koma ndi iye amene abwera ku chiwiri m’dziko monga Buroozi…lero kodi palichikaiko ca kuti Mulungu watuma Mtumiki woyela kachiwiri ku Qadian ?

(Kalimat Alfasl p.104-105. Review of Religions Qadian March 1915).

 

“Tsopano ndi chicodziwika kuti kukana Mtumiki  woyela ndi KUFR ndiponso kukana Messiah olonjedzedwa ndiponso KUFR, chi*****wa Messiah sasiyana ndi Mtumiki woyela. Koma ndiye  ngati iye akana Messiah sali KAFIR terenso amene akuna Mtumiki  woyelanso kafir, Mulungu aletsa.”

(Kalimat alFasl p.146-147. Review of Religions Qadian, March- April 1915).

 

“Kodi kuli cikaiko cotsala cakuti Mulungi watuma Mtumiki (pbuh) kwa chiwiri mu Qadian ku nsimikiza chilonjezo?”

(Kalimat al Fasl by Mirza Basheer Ahmad. Review of Religions p.105, N° 3  Vol 14).

 

Mirza alingana ndi Mtumiki Woyela Muhammad

Inali njira ina yofuna ku zilinganiza ndi Mtumiki  woyera. Mirza anati :

“Aliyense yemwe asiyanika iye ndi MUSTAFA (pbuh) Sanandione ndipo Sandiziwa.”

(Roohani Khazain, vol  16 p.171)

 

Ololedwa kupambilako Qadiani, Al-Fazl analemba kuti :

“ Chikhaliro cha olengezedwa Maseeh (Mirza) nimaso mwa Allah ndi chikhaliro wa Mtumiki woyela (SAW). Mchikumbukilo china,mzosungidwa za Allah kulibe kusiana pakati pa Messiah olengezedwa ndi Mtumiki woyela (SAW). Koma onse agawana mpando olingana ndipo ali ndi dziko limodzi. Angakhale kuti nimakambidwe ali awiri, awa ali m’modzi ndipo olingana.”

(Al-Fazl, Qadiani, vol. N° 37 dated 1e  September 1915, as cited in Qadiani Muzhah page 207, ath edition-Lahore).

 

QADIANI KALIMA.

Mimalembedwa a oyamba zinapangitsa nikhulupiliro izi :

“ Mkubwela kwa Messiah olengezedwa, kusiyana kumodzi kwapezeka ndipo ndikwa kuti akalibe kubwela ka chiwiri kwa Messiah olengezedwa, mcitanthauzilo kwa’Muhammadur RassuLullah’ Atumiki chabe amusiku akumbuyoku anali anaikidwapo, koma mkubwela kwa chiwiri kwa Messiah olonyezedwa Mtumiki umodzi waonjezedwapo pa tanthauzo la Mohammadur Resoolulah’…tero kumva mu Islam ndi kalima yemweyu, kusiyana kwekha komwe kulipo ndi kwa kuti kubwela kwa chiwiri kwa Mtumiki kutanthauzo lache…sifuna kalima watsopano, chi*****wa Messiah wolonyezedwa sali opatuka kucokela kwa Mtumiki woyela monga ali kunena ‘Saara wajuodi wajoodahoo (Manthu wanga anasanduka munthu sanandine ndipo Sandizindikila’ … telo Messiah iye amene abwela ka chiwiri m’dziko lino kuzafalitsa chi Islam, lero sitifuna kalima aliyense wa tsopano  ngati wina anabwela ndiye kuti modzi tinafuna…telo onse muyenela kuganiza.”

(Kalimat Al-Fasl p. 158 na Mirza Basheer Ahmad).

 

Chi*****wa ca kubadwa kwa Messiah tiolenjezedwa (Qadiani Mirza) kusiana kwabwela (mcitantha uzo ca Kalimah). Akalibe kubadwa Messiah olonjezedwa (Qadian Mirza) m’dziko monga Mtumiki, Mau akuti Muhammadur Rassolullah anaphatikiza mtanthauzo lawo, okhao aporofeti omwe analiko iye akalike kubwela; koma pambuyo pobwelanso kwa Messiah olonjezedwa (Qadiani Mirza) Kwa chiwiri m’maiko monga Mtumiki, Mtumiki umodzi waonjezedwa ku tanthauzira la Muhammadur Rassoolullah. Lero mkulinganandi kuukanso kwa Messiah olonjezedwa Kalimah, Mulungu akana, sikuthesedwa kuna kuwala kuposa. Mwa chidule, Kalima ameneyu ali ndi mphawu m’mpingo tsopano polowa  MuchiIslam. Kusiyana kwache kwa  kukhalanso ndi thupi la Messiah olenjezedwa (Mirza Qadiani) aonjezela Muhammadur Rasoolullah.” (Kalimatul Fasl page 158, Mirza Bashim Ahmad  Qadiani).

 

Kuonjezelapo, angakhali kuti tivomera pakuganizira zomwe sizingacitike zakuti zina lolemekezedwa la Mtumiki(pbuh). wolonjezedwa mu kalimah chi*****wa cha kuti ye ndi othela wa atumiki, angakhale lero palibe choipa ndipo sitifunanso Kalima watsopano chi*****wa cha kuti Messiah wolanjezedwa salipayekha kuchopa pa Mtumiki pakuti iye (Mirza) yekha a kuti; “ Ine ndi chimodzi-modzi ndi Muhammadur Rasoolullah.” Ndiponso “Iye amene a patula pakati pa ine ndi Mustafa Sandidziwa ndipo Sandiona.”

Chomwe wamkulu Allah analonjeza, cha kuti  azambwenzanso”Khatam-un-Nabiyeen m’dziko lino ka chiwiri monga Mtumiki  momwe olonjezedwa Mtumiki Messiah (Mirza wa Qadiani) mwa iye Muhammadur Rasoolullah, amene anabwelenso mdziko kaciwiri kumwaza uthenga wa Islam. Lero sitifuna Kalima watsopano.

 

QADIANI DUROOD SHAREEF

“ Lero mkulingana ndi malembedwe a Qur’an, ‘anthu achikhulupiliro’ tumani Salaat yanu kwa iye ndipo mulambile iye ndi ulemu (33:56) ndipo mkulingana ndi ma Hadiths amene muli malamulo atumila Durod kwa Mtumiki woyela pbuh, kutuma Durood kwa Hazrat Maseeh Dawood nkofunikila momwe muliri kofunikila kwa Mtumiki woyela pbuh.”

(Risala Durood Shareef-Mohd Ismael Qadiani p.136).

 

Mkulingana ndi zikhulupiliro za Islam ndi ma Hadith, nkojunikila kuonjezela M’baja lache (Mtumiki woyela pbuh) mu Durood. Chimodzi-modzinso nkofunikila kutuma Durood kwa Maseeh ndipo osakhala okhutila ndi Durood yomwe iya m’fikira iye (Mirza) angakhalenso ngati wina watuma Durood kwa Mtumiki woyela pbuh. Telo Hazrat Maseeh Mowood akuti :

“ Chimodzi pa zimene zikanidwa ndi ayah amene (Mirza) agwilitsila kwa iye ma akuti ‘alaihe assalato wa assalam ndipo kunena telo ndi HARAM. Yankho kwa ici ndilakuti ine ndine Mtumiki wolonjezedwa, ndipo ndiika pambari zikambidwa za Salaat and Salaam, Mtumiki woyela iye anati  amene amupeza, apeleka Salaam lache kwa iye ambiri, Salaam-o-Salaam yothokozera  Messiah olonjezedwa.

Pamene mau otelewa okhuza za  amenewa ndi Mtumiki, sahabah anati, Mulungu ndiye anati,lero chingakhale bwanji haram jama’at yanga kunena mau otelewa kunenela ine.”

(Risala Durood Shareef, Arba’een N° 2 Roohani Khazain vol. 17 p.349).

 

Mirza atengela zilembedwa za Qur’an Loyela.

 

Uyu munthu ozinenela yekha kuti akonda Mtumiki woyela mothelatu anayamba ziululidwa mwa woyela Mtumiki Muhammad (SAW) kumuululika kuti zonse zolembedwa ziululidwa mwa Mirza Ghulam pa ulemelelo wache.

 

Ngati mwatsegula mu Haqeeqatul Wahy mu Volume 22 la Roohani Khazaini muzapeza kuti pa matsamba 77 kufikila tsamba 111. Mirza Ghulam anena za ziululidwe zace maka-maka mchitundu cha Arabic. Omwe adziwa zilembedwe za Qur’an azadzindikila mwa muisanga za kulengela kwa matembedwe a bukhuli. Mkati mwa zolembedwamo, muli ziululidwe zomwe zinalembedwa kuthokoza woyela Mtumiki Muhammad ndi zina zinagwilitsidwa  Hazrat Ibrahim (AS). Ndi dzitsanzo cabe zingono zomwe ziza kambidwa.

 

Allah athokoza Mtumiki woyela Muhammad (pbuh) ndi anzake mu Qur’an loyela m’malembechwe awa :

“Muhammad Rasuulullah wal ladhina m’ahuu, ashiddau’alal kuffur rahman bainahuù.”

Muhammad, mtumiki wa Allah ndi aja omwe ali naye.  (Al-Qur’an 8-29)

 

Mu zaka zikwi-zikwi zapita kumbuyo uku, Ma Muslims sana khale ndi chitanthaulilo china cha verse kapena zilembedwezi koma WAHI wa Mirza amvuza kuti :

“ Muhammad Rasoolullah wal Ladhiina m’ahuu ashiddan’ala kuffaar whaman bainahum mchiutlidwe ici Mulungu andipatsa dzina lakuti Mohammed ndipanso Mtumiki.” (Roohani Khazain vol 18 p.201)

 

Zotsatira ndi nindakaturo za zilemedwe za Qur’an loyela zomwe ense mu Muslim okunda Mtumiki adzadzidzi ndikala mwamsanga kuti athokoza Syedna Muhammad (SAW), zinaulidwanso kaciwili kuthokoza Mirza Ghulam Atelo Mirza :

“ ‘Huwa Iladhi arsala rasuulahu bil huda’ Iye mulungu neliye watuma mtumiki ndikumulangiza zacita.” (al-Qur’an p:33)

 

“Subhana Ilahi asraa bi’abdihii…alemekezedwe Allah amene anatenga kapolo wache usiku pa ulendo wopita ku Masdjid AlHaram kupita ku Masjidal Aqsa…” (al-Qur’an 17:1)

 

“ Qul in kuntum tuhibbunallaha fatabiun” akuti (O Muhammad) Ngati umukonda zoona Allah, undilondele” (al-Qur’an 3:31)

 

“ Inna fatahua laka fata-han mubiina.” (al-Qur’an 48:12)

 

“ ‘Ya Siin walaalin Hakim. Innaka la minal murSaliin… Yassen ! Zoona inu Muhammad muli m’modzi mwa atumiki.” (al-Qur’an 36:1-3)

 

“ ‘Inna aatainaakal Kawsar…’ Tamupatsaini inu mtsinje mu paradiso…” (al-Quran 108:1)

 

“ ‘Wa arsal naakal ila rahmatan lil aalamiina.”

Ndiponso sitinakutume kuti ukhale wachifundo kwa onse ni calo.” (al-Qur’an 21: 107)

 

Atatenga udindo wa woyela Mtumiki (SAW), anayamba kudzipatsa iye tyekha uzidindo wina :

·         Mbanja lace linakhala AHLE BAIT

·         Anzake anakhala a Sahabah

·         Mkazi wace anakhala umm-ul-m’OMINEEN

·         Mosque yomwe inamangidwa ndi atate ace inakhala al-AQSA MOSQUE QADIAN.

 

Kwa zaka zikwi-zikwi (1400 yrs) a Muslim sandziwa bwino za zobisika za dziko loyela la Jerusalem. Ndipo mkulingana ndi Mirza Ghulam Masjid Aqsa, Qadian Mtumiki woyela anapita ku Qadian osati ku Jerusalem pa usiku wa Ascension Mirza akuti :

 

“ Munalembedwe mu Qur’an loyela (17:1) ‘Subhan alladhii asra bi’abdihii lailammin al Masdjid al Haram ila al Masdjid alAqsa…’ Ulemu kwa iye amene anatenga kapolo wace usiku kunicotsa kwa Masdjid Haram kumpereka kwa Masdjid Aqsa…Kutanthauza kuti Mosque inamangidwa ndi atate ake a Mirza ndipo ku kulitsidwa kwace kwapangidwa ndi Mirza.”

 

Qadiyan inakhala yocilizidwa monga ARDh-e-JARAM ndipo kuyendela malowa kunakhala cithoozi cha Hajj:

“ Malo a Qadian  ndi lemekezedwa. Khamu la anthu lalipanga kukhala malo a Haram.” (Mirza Ghulam’s poetry Dur-e-Sameen p.58).

 

Anthu anapita ku superogatory (Nafy) Hajj. Koma kumalowa (Jalsa Salama mu Qadian) ndipo lace ndilopambana NAFIL HAJJ ndipo kusaikila nzelo sikwabwino pakuti njila yake (Ahmadiyya) ndi yabwino ndipo zamtendere zichoka kwa Mulungu. (Alna-e-Kamalat-e-Islam. Roohanni Khazain vo. 5- p.352)

 

Pakuti okhao amene ali olemela ndiamene akwanitsa kupita ku Haji, osauka amewa lephela kupitako.Lero Mulungu waikapa ZIL HAJJ kotelo kuti aja omwe ajuna kutukuta chikhulupililo cha Islam ndi aja osauka a Muslim a ku India naonsO angapezekeko.” (Khutba Mlan Mehmood Ahmad Khalifa Qadian, Pepala la Alfazl vol.20 N°66 lolembedwa pa 9 Dec. 1932).

 

Ndipo Pothela, koma osati chothelelela, omwe anatenga mpando pambuyo pake anakhala “Khulafa-e-Rashideen.”

 

Wahi la Mirza Ghulam

Pa nthawi Mirza anatha matha ndipo anali kukamba momasuka za zikhulupiliro zace. Telo anaulula za WAHI lake.

“ Chomwe chipangitsa zikhulupililo zathu si Hadith ichi koma Qur’an ndi Wahi yomwe ibwela kwaine. Inde, nikuonjezako tilangiza aja ma Hadith omwe ali nikulingana ndi Qur’an ndipo satsutsana na WAHI langa. Ma Hadith ena, ndiataya kutali monga pepala ilibe nchito.”

“ Mu Braheen-e-Ahmadiyya, Mulungu aniitana nidzina la Ibrahimu.” (Arba’een n° 3. Roohan Khazain, vol 17 p. 420).

 

“Zophunzitsa zanga ziphatikiza malamulo ndipo ziletsedwa ndi zifunilo za Shari’at. Pa chi*****wa ici, Mulungu apatsa dzina Wahi yanga ndi zomwe ndi chita lakuti ‘bwato’. Telo unani ndi zikhulupiliro zanga ndi kuti ndine chombo cha Noah ndi chopulumukilamo cha anthu onse. Lekani yemweali ndi matso aone ndipo amene ali ndi matu anvele.” (Arba’een vol. 4 p.6 Roohani Khazain vol. 17 p.435).

 

“ Ndinena molumbila kwa Mulungu kuti ndikhulupilila mu zomwe ndichita monga momwe ndikulupililanso Qur’an ndi mabukhu ena a Mulungu. Monga momwe ndikhulupilila Qur’an mosakaika kuti ndi bukhu la Mulungu, Chimodzi-modzinso ndikhulipilila kuti Wahi ija yomwe itsika mwa ine ndi Mau a Mulungu. (Haqeeqat) Wahi Roohani Khazain vol 22 p.220)

 

“Chikhulupililo changa mu Wahi chilingana ndi chikhulupililo comwe ndili nacho mu Qur’an ndi Torah.” (Haqeeqatul Wahi, Roohani Khazain vol.22 p.401)

 

Mirza ndiopambana pa Mtumiki woyela Muhammad SAW (ma’azAllah):

Mirza Ghulam Ahmad anali akali osakhutila. Anali kufuna kupitililapo. Chomwe anacita cholondolapo chinali chozikutitsa kupambana Mtumiki woyela Muhammad (SAW). Ndipo anati :

“ Koma ceni-ceni ndi ca kuti za uzimu za Mtumiki woyela  pbuh (mwa Mirza Ghulam) Kuthela malemba ya chisanu ndi kamodzi, ndi zamphamvu kwambiri mkulinganiza ndi zaka zakumbuyoku. (Khutba-e-Illhamiah, Roohani Khazain vol.16 p.271)

 

Za nzimu za mporofeti wathu oyela (SAW) zinali zobisiku mu 5th thousand (Makk’i birth) ndipo nthawiyi sinali yapamwamba mkukula kwa zauzimuwace. Koma uku kunali koyambilila kufika pa mwamba-mwamba pa tsanja ya zabwino. Pambuyo pace, za uzimuzi zinafika pa chimake mu 6 th thousand (Kubadwanso kwace mu Qadian) pa nthawi imeneyi. (Mirza in Khutba-e- Ilhamiyah, Roohani Khazain vol. 16 p.266).

 

Anthu omwe anali kumtsata anawauza kuti anapatsidwa zi zindikilo ndi zodabwitsa zokwanila 300 000 pamene Mtumiki woyela anapatsidwa cabe 3000. Mozikuza yekha, analemba kuti : “Kwa Mtumiki woyela, Mulungu anamuonetsa cabe eclipse ya Mwezi. Koma ine anionetsa Ma Eclipse yonseya Mwezi ndiponso ya dzuwa, lero kodi simudzandikhululupililila?” (Aijaz-e-Ahmadi, Roohani Khazain vol.19 p.183)

 

Ananena kuti zambiri zobisika za mu Qur’an kapena zinanthauzo za cinsinsi sizinachulidwe kwa Mtumiki woyela (SAW) koma iye wauzidwa pa izi. Tele Mtumiki woyela sanadziwe tauthauzo la Ibne Maryam, Dajjah, Donkey dajjah, Gog ndi Magog, Daabah) Ardh. (Izala-e-Auham, Roohani Khazain vol 3 p.473).

 

“Uisilamu wa Mtumiki woyela unaoneka ngati  Mwezi wa tsopano (Mthawi ya Mirza) ndipo unali kuyembekezedwa kasanduka monga mwezi odzala.” (Roohani Khazain vol 16 p.184)

 

“ Nchodziwikilatu kuti Fath-e-Mubeen anabwela pa nthawi ya Mtumiki wathu ndipo kupambana kwima kunatsala komwe kuli kwa kukulu ndi kodziwikilato ndipo nthawi yace ndi nthawi ya Messiah wolonjezedwa.” (Roohani Khazain vol.16 p.288).

 

Chinenedwe ici cinanenedwa pamatso pa Mirza ndi anthu omwe anali kunitsata. Kwanenedwa kuti Mirza anati : Jazakallah ndipo atalemba malembedwe a bwino, anapachika zolembedwazi m’nyumba yace.

 

“ Muhammad watsikanso pa ife ndipo ndiochuka kuposa kale. Amene afuna ku muona iye bwino-bwino ayenera kuyangana Ghulam Ahmad mu Qadiyan;.” (Qazi Zahoor Ahmad Akmal Qadiani yolembedwa mu pepala la Paigham-us Sulh- 14th March, 1916).

 

“ Kukula kwa nzeru kwa Messiah wolonjezedwa (Mirza of Qadian) ndi kupambana Mtumiki woyela (pbuh). Iyi ndi mbali cabe ya kukula kwa Messiah wolonjezedwa kuposa Mtumiki woyela.”

 

Mirza apatiliza kumcepetsa Mtumiki oyela Muhammad (SAW).

 

Mtumiki woyela sanadziwe tanthauzo la Surah Azilzal (Roohani Khazain Vol 3, pp;166-167)

Zomwe anaulula Mtumiki woyela zinasanduka zaboza. (Roohan Khazain Vo l3 p.472)

Mtumiki oyela analakwa mkumvetsa kwa zouliludwa (Roohani Khazain Vol 2 p.224).

 

Manda a Mtumiki woyela ndi malo oyopedwa kwambiri ndi a Muslim dziko lonse.

 

“Lero Mulungu anatsankha malowa kuti aikepo Mtumiki  woyela (pbuh) omwe anali oipa ndipo onunkha kwambiri ndiponso  wamdima, malo umwe anali odzala ndi matubvi atidoyo…” (Roohani Khazain Vol 17 p.205).

 

Akuzipanga kuti ndiye Mtumiki othela.

 

Pa nthawiya, Sichinali choodabwitsa kuti anali kunena kuti ndi Mtumiki othela.

“ Mwa nthawi zambiri ndakhala ndiri kunena kuti nikulingana ndi verse, ‘Wa aakhareena minhuru lamma yalhaguo belim-ndi ena omwe akalibe kuzionjezela pa iwo…’ (al-Qur’an 62:3) mu BUROOZI, halili Mtumiki m’modzi-mdozi KHATUM-UL-ANBIYA (othera wa Atumiki). Zaka makumi awiri apita kumbuyoku Mululngu ananicha Muhammad ndi Ahmad mu Braheen-e-Ahmadiyya ndikunena kuti ndine Mtumiki woyela (pbuh) omwe atenga nalo a Mtumiki emwe analipo. Lero Utumiki wanga siutsutsana ndi Utumiki wa Mtumiki woyela (pbuh) wanga Mtumiki  wothela chi*****wa cha kuti nkosatheka kupatula cithunzi, kuchoka ku chinthu chomwe chapanga chithunzico pakuti ndi chinthunzice cha Muhammad, lero ndiri Mtumiki wotsiriza pakuti Utumiki  wa Muhammad unatsala ndi Muhammad.” (Mirza Ghulam in Ghalti ka Izala, Roohani Khazain vol 8 p.212 ).

 

“ Niodala iyo amene andidziwa . Pa njila zonse zopita kwa Mulungu ine ndine njile yothela, ndipo pa zowala zace, ine ndine njila yothela, ndipo pa zowala zace, ine ndine kuwala kokhela. Koma tsoka kwa iye amene satsata ine ci*****wa chakuti popanda ine, zonse zili munidima.” (Kashti-e-Nooh, Roohani Khazain vol 19 p.61 ).

 

“ Ndine ndekha demwe wasankhidwa mu Ummah kutenga dzina la mtumiki.” Palibe wina aliyense amene angapatsidwe dzinari…ndipo dzinari kufuna kuchitidwa…monga momwe zinanenedwa mu Sahihi Hadith kuti kuzakhala cake munthu ekhayo nimodzi ndipo  chinenedwechi chatsimikizidwa.” (Haqiqeetul Wahy; Roohani Khazain Vol 22 p.401).

 

Umtumiki unathela pali mtumiki wathu (pbuh). Lero mpambuyo pace palibe Mtumiki  wina  kuchotsako yemwe wakudziwa ndi kuwala kwace ndipo wapangidwa kutenga inalo ace ndi Mulungu. Dziwani kuti kumathelo kunapatsidwa kwa Muhammad (pbuh) kucoka pa chiyambi  ndiku patsidwa kwa iye (Mirza) amene anaphunzitsidwa ndi uzimu wace ndikumupa chithunzi cace. Lero diodala amene aphunzitsa ndiponso  ndiodalanso amene amphunzira (Mirza) . Lero Mthero anaikidwa mu Malembamu ya chisanu ndi  kamodzi. (Zamima Khutba Ilhamiah, Roohani Khazain vol 16 p.310).

 

Mirza BasheerAhmad s/o Mirza Ghulam analemba kuti:

“ Lero munthu m’modzi yekha anatenga udindo wa Utumiki mu Ummah wa Muhammad… kucotsako cabe Messiah walonjedzedwa (Mirza) kulibe wina analondola Mtumiki  woyela. Motelo, ndi Messiah olonjezedwa cube amene anasankhidwa kuchedwa mporofeti.” (Kalimat Al-Fast, Review of Religions, Qadian p.116 N° 3).

Magazini yololedwayo Qadiani analemba kuti :

“ izi zolembedwa  zionetsa kuti ndi Messiah cabe wolonjezedwa amene angakhale Mtumiki… Pambuyo pa mporofeti oyela (pbuh) Mtumiki nimodzi cabe anali kufumka ndipo kubwela kwa a Mtumiki ambiri kunakazokoneza zifunilo za Mulungu ndi zomwe anali kufuna kucita.” (Tasheed-ul-azhan, Qadian, n° 8, vol 12, pp.11, August 1917).

 

Mirza Adzudzula Islam

CHI  ISLAM   CHOMWE  CHINALIKO   MIRZA   AKALIBE   KUBWELA NDI CHI ISLAM   CHAKUFA

 

Maka-maka mu chaka  cha 1906, mwa maganizodwe a Khwuja  maluddin, Moulvi Muhammad Ali analowa nchigwilizano ndi mkulu wa Akbar-e-Watan (wowona pa zilembedwe) kuti aone kuti zolembedwa zao siziulutsa za cikhulupililo ca ka guru ka Qadiani. Zolembedwa zinali kufunika chabe kuulutsa za cikhulupiliro cha Islam. Olonjezedwa Maseeh anakana zamaganizo awandiponso a Jamaat naonso, Hazrat Sahib anati.”

“ Muzanena za Islam mu dziko mosandiikako ine?.” (Zikr-e-Habib by Mufti Muhammad Sadiq Qadian p.146. First Edition).

 

“ Tikhulupilila kuti mpingo yomwe alibe chiphupirio cha Utumiki (Monga mu Islam) ndi mpingo yakufa. Tunanena ma religion ene monga ma Yahudi, ma christu  ndi ma Hindus kuti ndi m’mpingo yakufa chi*****wa cha kuti alibe Mtumiki .Kodi nchi*****wa ninji tinena kuti Islam ndiyopamnana pa m’mpingo ena onse ?” Iyenela kuti isiyane.” (Malfoozat-e-Mirza, Vol.10 p.127).

 

MIRZA ANENA KUTI ISLAM NDI YACABE-CABE NDIPO NDI YA USATANA

 

“ Kuti mpingo si mpingo ndi Utumiki si Utumiki pakulondola munthu amene salipafupi ndi Mulungu kuti apatsidwe mphamvu zace. Kuti mpingo ndiwa chabe-cabe yomwe uphunzitsa anthu kuti chitukuko cha munthu chiyembedwa cabe pa zomwe zilembedwa mu Qur’an loyela ndi mu Shari’at-e-Muhammadia yomwe inanenedwa ndi Mtumiki woyela (pbuh) ndipo kuti ‘WAHI’ yatsata mu mbuyo m’malo mopita pa tsogoro… lero chimpingo chotere  chiyenekela kuchedwa kuti ndi chansatana osati cha  Mulungu. (Zamima Braheen-e-Ahmadiyya, part  V. Roohani Khazain Vol 21 p.306).

 

“ Ndi chodabwitsa kukhulupilila kuti pambuyo pa Mtumiki woyela (pbuh) Chitseko cha ‘wahi’ chatsekedwa ndipo kulikenso chiyesezelo chanaco mpaka tsiku loika-lamba cabe . Kuli mpingo yomwe sikhuzana ndi wamkulu Allah yomwe ingachedwe mpingo ?… ndinena mwa Mulungu wamkulu, kuti nimasiko ano, kulibe amene ati nkhidwa kopambana ine mu mpingo yotere. Ndinena mpingo wotereyi  ndiusatana  ndipo  kuti   mpingo   ya  jehena  ya  kumoto ndikutseka maso a munthu mpaka kufu kwache.” (Zamina Braheen-e-Ahmadiyya part V).

 

MIRZA NDI QURAN YOYELA.

 

“ Qur’an ndi bukhu la Mulungu ndi mau amukamwa mwanga.” (Adversement dated 15th March 1897, Roohani Khazain vol 22 p.87).

 

pamene Mirza Ghulam Ahmad anaudzidwa kuti zolembedwa zace zinyoza aja amene anali kutsutsana naye, anane kuti Qur’an nayonso ili ndimau ambii vipa ndipo anafotokoza kuti sanali kufikako pa zofunikila za masiku ano. (Roohani Khazain Vol 3 p.115-117 ).

 

ZOSINTHIDWA   MU   QUR’AN   YOYELA

 

Pali njira zambiri zomwe izi zingantidwe:

Kusintha  kwa mau

Kusintha  kwa zitanthauzo

Kusintha  kwa zindime

Kucotsa zikakamizo za Qur’an

 

Mirza Ghulam Ahmad anapezeka ndi milandu yonse inai. Angakhale kuti sanasithe ziri zonse zolembedwa mu Arabic m’bukhu la Qur’an, koma m’malembedwa ace ocotsa mbukuli, asintha mwadala zina zolembedwa mwa Arabic. Zitsanzo za zina za lembedwa mu matsamba otsatila.

Chitsanzo chodziwika kwambiri pa zosinthidwa za matanthauzo a Qur’an loyela ndi ndime la 3 : 144  lomwe linene  pa KUTHA KWA UTUMIKI

Kuchoka pa chiyambi cha Islam, pa nthawi ya Mtumiki  woyela Muhammad kufikira lero lino, onse ma Muslims anaciona chinthu chosasokoneza pa MirzaGhulam Ahmad yemwe mu zaka zoyambilira anali ndi chikhulupiliro chotere. Koma pambuyo pace pomwe maganizo ace anasintha, anapatsa chinenero chotere cha kuti Utumiki wa Muhammad siunathero koma masegulidwe a Mtumiki amtsogolo, Monga kuti ALLAH, yemwe  anatumiza Atumiki 124.000 la amupatsa udindo Mtumiki woyela Muhammad. Atero anena kuti ndiye adzakhala Mtumiki wotsatiripo, kuunika kokhera pakati pa kuunika konse kwa Allah. M’manenedwe ena, zonse zokambidwa zosokoneza mitu zomwe anapatsa m’mabukhu ache mu ndime imeneyi zinali zofuna cabe kupititsa pa tsogolo Utumiki wace. Atsegula chitseko cha KHATME NABUWWAT, alowa ndiponso atsekanso. Kodi sichitsanzo cha chikuri chakuba chimeneci ?

 

Chimodzi-modzi owelenga zoleyembedwa  kuti anawelenga momwe ndime zotamanda Mtumiki  woyera Muhammad SAW zinasinthidwa ndi Mirza.

Kulakwira kwa JEHAD ndi Mirza Ghulam Ahmad ndi chitsanzo chutuma kuyesa malamuro a Qur’an. Tingagwiritse nchito chilembedwe Chimodzi.

“ Kucoka lero jehadi ya munthu yomwe icitidwa ndi panga, linakwilidwa ndi kulamulidwa kwa Mulungu. Kuyambila lero, aliyense amene anyamula panga kunyamulura kaafir ndi kuziyitana iye kuti ndi GHAZI ali ku lakwira otumidwayo (SAW), amene ananena kwa zaka 1300 zapita kumbuyo  kuti pambuyo pobwela Messiah olenjezedwa onse ma jehads ali ndi ma panga azatha. Telo pakubwela kwanga KULIBE JEHAD ALIYENSE AMENE ALI NDI PANGA. (Collection of Advertisement p.295, vol.3 ).

“ Kochoka pomwe ndinali mwana kufikila lero pomwe ndiri ndi zaka 65, ndakhara ndiri kugwira nchito ya cholembetsa ndi lirime langa pakufuna kusintha m’tima ya ma Muslim’s kuti akhale a chikondi, a chikhulupiliro ndi a chifundo kwa boma la British ndikucotsa ganizo la jehad m’mtima ya Aslims opusa.” (Kitab-ul-Bariya, (Roohani Khazain Vol 13 p.350).

 

“…Mmalo  Boma la  Azungu (British) ndaulitsa ndikufalitsa timapepala 50,000 mdziko lino (India) ndi maiko ena a chi Islam kudzudzula Jehadi…zokoma zake ndi zakuti anthu masauzande ambiri asiya maganizo ao oipa a jihad.” (Roohani Khazain Vol 15 p.114).

 

Mirza ndi Asilamu

Munthu wina anafunsa funso pa za ma Muslims ndipo Mirza anayankha motere ndipo yankhoyi ifunika ku welenga. Zonse ziwiri zinalembedwa mu bukhu lache, Haqeeqat-up-Wahy:

“Funso : Huzoor-e-aali anena mmaro ambiri-mbiri uti sichili chofunika kuyitana KAFIR kuti Kalima-jo (Mnthu amene anayeselela Kalima) ndiponso Ahle-Qibla. Ndi chodziwikilatu  kuti muchitsazo chi, Momineen amene anakhala Kafir pokukana, koposa kumvomelera iye, palibe amene akhala Kafir. Koma mulembe kwa Abdul Hakeem Khan kuti aliyense amene alandila uthenga wanga.

Koma sanandikolole kapena kundivomela ine, iye Muslim. Kuli kutsutsana pa mava awa ndi mau omwe analembedwa kumbuyoku. Poyambilira mu Tiryaqul-Quloob munanena kuti palibe amene akhara Kafir posakukumbukirani koma tsono mulemba kuti pa kukana inu, iye akhala Kafir.

Yankho: Ndi chodabwitsa kuti mpinga munthu amene akana ine ndi munthu amene iatana ine kuti Kafir  ndi anthu osiyana, pomwe mmaso mwa Mulungu ndi munthu m’modzi; chi*****wa amene akana ine  chi*****wa cha kuti azonda ine. Mingu Munthu wabodza-kuchotsako ichi, iye amene sandilora sakhulupirira mwa Mulungu ndiponso mwa Mtumiki. (Haqeeqat-ul-Wahy, Roohani Khazain Vol 22 p.167).

“Kuchotsako ANA ANTHU ACHIWERE-WERE, omwe mitima yao ndi yotsekedwa ndi Mulungu, aliyense akhulupilila mwa ine. (Aina-e-Kamalat-e-Islam, Roohani Khazain Vol 5 p.547).

 

“Mulungu a ndiuza  kuti ali yense emwe walandira uthenga wanga ndipo sanandimvomera, ameneyu sali mu Muslim. (Kalata ya Mirza kwa Dr Abdul Hakeem Khan Patialvi)

 

“Ndiri ndi chifuniro cha Mulungu cakuti iye amene sakulondola ndiponso sazalowa mu B’ith yako ndikukhala otsutsana ndi iwe kapena mdani wako, alibe ulemu kwa Mulungu ndi kwa Mtumiki, Hellish;” (Advertisement mu M’ayaar-ul-Akhyarya Mirza Ghulam p.8)

 

“Lero kumbukirani momwe Mulungu andiuzila kuti ndi chosaroredwa kupemphelera kumbuyo kwa emwe sakhulupilila ndiosafuna, koma kuti Imam yako akhale umodzi wa iwo.” (Arbaeen n° 3, Roohani Khazain vol 17 p.147 just note).

 

MATHERO

Kwa Owelenga!

Ndikhulupilira pa nthawi ino mwaona chomwe munthuyu anali kulingalira. Kudzionetsa kwa kuti anali ndi chikondi cha chikuri cha Utumiki wa UIslam kunali kudziwa lingo lache kuti atsate guru la Ahmadiyyah. Mafunso omwe muyenera kuzifunsa inu nokha ndi aya;

Kodi zilembedwe za m’bukhuri ndizoona ?

Ngati ndizoona, nanga Mirza Ghulam Ahmad, amene anayamba Ahmadiyyah  anamuyamika mwachoonadi Syedna Muhammad kapena anamunyoza?

Kodi munthu woteleyo ndi olongosoka ?

Ngati nitelo, kodi munthu oteleyi tinganene kuti ndi mu Muslim ?

Nanga nchiani chomwe chipangitsa agulu la Ahmadiyya  kubisa izi zokhuzana ndi munthu amene anayamba gururi ?

Kodi Ahmad ndiolondola weni-weni wa Mtumiki  woyela SAW ?

Kodi ameneyu anali munthu otani ?

Angakhale ziganizo zanu zikhale zotani, Mirza Ghulam Ahmad iye izinena motele:

 

Ndiri unyolo mzanga ! Osati munthu, ndili mbali yosaoneka ya munthu ndi malo mvetsa manyazi ku anthu. (Tanthauzo La mau mu Urdu ndi malo yabisika ya anthu olemba)

(Braheen-e-Ahmadiyya V, Roohani Khazain vol 21 p.127 ).

Tipempha Allah aonetsa kuwara kwa Islam ku onse omwe anasochela chi*****wa cha zi chilidwe zotelezi mu dzina la Islam. Allah achinjilize chikhulupililo cha ma Muslims onse ku zoipa zoterezi.

Ameen.

Mtendele ukhale kwa iwo amene olondora njira yoona. 

ANTI AHMADIYYA MOVEMENT IN ISLAM

SYED ABDUL HAFEEZ SHAH

DR SYED RASHID ALI

P.O BOX 11560

Dibba Al Fujairah

United Arab Emirates

Fax (9719) 442846

http://alhafeez.org/rashid/

rasyed@emirates.net.ae

 



» تاريخ النشر: 26-11-2009
» تاريخ الحفظ:
» شبكة ضد الإلحاد Anti Atheism
.:: http://www.anti-el7ad.com/site ::.