عرض المقال :Religious Adventurism
  الصفحة الرئيسية » مـقـالات الموقـــع » كشف البلية بفضح الأحمدية » Non - Arabic Articles » Nayanga/Chichewa

اسم المقال : Religious Adventurism
كاتب المقال: webmaster

 

Anti Ahmadiyya Movement in Islam

 

CHIPEMBEZO NDI TSONGAZACHE MUCHI ISLAM

TAHIRA PARWEZ

Asilam amakhulupilira ndi kutsatira Muhammad (S.A.W) kuti ndi mtumiki omaliza,

ndiposo quran ndi Buku lomaliza, kuchokera kwa Allah. Yense omwe atasintha liu

kapena mau amumabuku opatulika ai akankhidwa patali ndi chipembezo cha chi Islam.

Chi Islam, monga zipembezo zinazache, zilindi tsongazache zomwe zimasunga

ulemelero wache kuza chinyengo monga aneneri onyenga uchokera chiyambi

chazipembezo. Zambiri mwaizi zipembezo zo nyenga mwaturuka zinthu zo nyasa anthu

ndi ku zikana koma ambiri ndiochenjera kenaka zeru za ndale kumaesa kuti aike

muchipembezo. Mau ochokera kwa Allama Iqbal Mundizo tizaona umu. Chi*****wa

chopezeka gulula (MULLAHISM) kuonoengeka kwa chipembezo pamodzi ndi azibusa

ndi Aslam chi*****wa chamsokonezo, ndi aneneri onyenga.

Musaylima, Sadjah, Al-Aswad al-Ansi ndi Tulayha bin khuwaylid onsewa nthawi yao

anadzicha aneneri pambuyo atamwalila Muhammad (S.A.W) awa onse amaitanidewa

kuti ndi (Ridda) omwe sakuvomera lamulo kuchokela ku Medina chi*****wa chokanira

mitundi ndi kusankhana kwamadera. Al-Aswad (wa chinyengo) anali msogoleri oyamba

wa (ridda) dziko la Yemen. Wa chinyengo yu sakudziwika ngati adali mu Islam.

Chi*****wa anali lyeyu wa maloto monga ng’anga yamaula (Kahin). Iyeyo anali

kunyengeza anthu mdzina la Mulungu (Allah) anali kuombeza ndi dzanja lache.

Pambuyo pa kupha umodzi wa kwao (Sahar) ataona akhale iye mmalo mwa Muhammad

(S.A.W), anakhala pautsogoleri uyu Al-aswad mneneri onyenga miyezi yochepa kenaka

mkadzi omwe anakwatila dzinalache ndi (SAHAR) anaganiza zakupha mwamuna wake,

pombo Al-Aswad anaphedwa.

Musaylima (Al-Kazab) anazicha mneneri onyenga nayenso pambuyo pa kufa kwa

(Howda) anafunisitsa kuti naeso akhale msogoleli wa (Banu Hanifa) chaka 630 AD iye

yu amapanga zamapemphero kataatu basi patsiku, kumanga kusiyakudya ndikusiya

pangono kumwa vinyu (Wine). Analiso okhulupilira kuti munthu akamwalira azauka

kwakufa. Analemba kalata kwa mtumiki wathu Muhammad (S.A.W) chaka cha 632 AD

kufunitsitisa kuti naenso amulole kukhala mneneri, koma mtumiki Muhammad (S.A.W)

ana kana ndi kumzuzula. Nthawi yomweyo Abubakari (RTU) anatuma Khalid Bin Walid

(RTU) pamodzi ndi asikari ambirimbiri kuti akagwebane nae. Kenaka asana mwalire

mkadzi wake anali ndi (SAJDAH) pomweo Musyalima anaphedwa. Naeso mkadzi wake

ana zicha mneneri pambuyo pakufa mwamunawake, kulalikira mtundu wao wa

(TAMIM)

Al-Harith bin Said naenso ana dzicha mneneri nthani yankhondo mtundu wa Ummayah

(Caliph), ABD Al-Malik bin Marwan. Asilikari ambiri naonso anali ogwirizana nae kuti

ndi mneneri. Koma anamkwanisa kumgonjetsa mpakana anamupha chaka cha 698-699

A.D. Immam abu Hanifa ndiwa chikhulupiliro kuti Muhammad (S.A.W) ndi mtumiki

 

womalidza (Khutum-E-Nubuwat) anapeleka (Fatwa) kuti muslam aliye nse omwe

azachoka mmalamulo achipembezo ndikudzicha iye yo mneneri, ai kulibwino abweretse

umboni ndithu okwana. Anthu ambiri ozicha aneneri onyenga ana chulukira munthawi ya

699-767 A.D. Tione nalonso gurula Shia uyu Al-Mukhtar bin Abi Ubayd nae anazicha

mneneri koma osewa ndi onyenga.

Muhammad bin said (Al-Muslub) naye anali mmodzi omwe anali osokoneza osintha ma

Hadith. Anaononga Hadith ndi kusintha sintha monga hadith iyi ndiena mahadith;- “Ine

ndine mtumiki omalidza kuribe wina azabwera ineyo ndita mwalira” iyeyu anaongezera

mauake kut:- “pokhapo Allah ankafuna kuika wina” naeso uyu anali kuzi cha mneneri

moonjezera mahadith chi*****wa chofuna kuononga chipembezo cha Islam. Abu Jafar Al-

Mansur (Caliph) wa Abbasid adalamulira asilikari kuti aphedwe, atafa uyu naeso Hashim

bin Al-Mahadi. Hashim anali ndi anthu omutsatira mumzindamo, kenaka anagwidwa ndi

kunyongedwa mchaka cha 779-780 A.D

Mahmud bin Al-Faraj nae anatulukira mumdzinda wa Samara mchaka cha 849-850 A.D

omwe anati Quran inafikila mwaiye kuchokera kwa Allah upitila kwa Gabriel. Nae adali

ndiomtsatira ambiri mumdzinda wa Samara ndi Bagdad. Kenaka sipanapite nthawi

anaphedwa ndi kunyongedwa, Caliph Al-Mutawakkil analamulira kuti aphedwe.

Mirza Ali Muhammad oitanidwa (bab) chitseko, iyeyu ana badwa chaka cha 1819 A.D

anali umoyo wake ku Shiraz, Iran. Anaphudzira pakana atafika zaka 15 anayamba nchito

yama londa pamodzi ndi amalume ake. Atafika zaka 22 ana kwatira ndi kubala mwana

wa mwamuna omwe anafa akali wachichepekele. MaShia palipose, amakhulupilira kuti

kuli ma Immam obisika monga mchaka 1260 Hijra (1844 A.D) 121 zinali panthawi ya

chisangalaro pomwe anasowa. Nthawi yomwe monga ya chisangalaro mwachizolowezi

chaka ndi chaka, Bab anazicha kuti iyeyo ndi Imam wa 12 onse akulu akulu ma (Sheikh)

ansembe anamulandira chi*****wa chaboza lache. Ambiri anayamba kudabwa naye

chi*****wa Imam wa 12 azakhala osiyana ma bweledwe monga (Hurqalya) sazabwera

monga munthu monga iyeyu.

Chi*****wa chochenjera kulankhula izindi izi ugonjetsa ose akulu ansembe, anati ndine

(Nuqtiyiula) mmodzi mwadzina la mtumiki Muhammad (S.A.W) naeso ati Quran ndi

(Sharia) malamulo tsopano asintha. Koma otsatira guru la Shia ndi Sunni makamaka

ansembe anamuyesa wamisala openga pomwepo adaponyedwa mdende nthawi ndi

nthawi kenaka analamulidwa kuti aombeledwe futi afe, chaka cha 1850.

Mirza Husayn Ali (Bahaullah) anabadwa mchaka cha 1817 mumdzinda wa Tehran.

Iyeyu anali mwana oyamba kubadwa wa Mirza Abbas waku Nur, Aduna yanyumba ya

malamuro. Anaphudzira akali mwana panyumba basi. Iyeyu anali pambuyo pa bab

naeso analowa mdende chaka cha 1852 chi*****wa chofuna kupha Shah. Bahaullah akali

mdende adali ofooka chi*****wa chamatenda kenaka adamthawitsira kudziko la Bagdad

kuti asanyongedwe. Adapulumutsidwa ndi anthu aku Rusia A Minister. Nthawi atafika

ku Bagdad, Asilam sanakondwe ndi uphunzitsi wake kenaka Mfumu yandodo inaganiza

kuti achoke mwao mu Bagdad adamuthamangitsa kuti apite ku Constantinople ndi ku

Adionople. Chaka cha 1863, pambuyo pomuthamangisa mu Bagdad, akali mjira anati

lerolino ndine mneneri ndi poso mtumiki wa Mulungu (kalingana momwe ananenera

Bab) koma osewa anavomera inde ndimwe mneneri, kotero ndife ma Bahais. Patapita

nthawi msokonezo unayamba pakati paiwo chi*****wa odzodza uneneri kuchokera kwa

Bab ayenera kukhala ndi Mirza Yah- ya osati Bahaullah ai.

 

Ose anthu anasintha ndi kutsatira Mirza Yahya kumusiya uyu onyenga Bahaullah komwe

ku Turk. Boma la Turk linapepha kuti onse otsatira Babi ndi Bahai achoke muno

mwathu mu Adrianaple. Koma Bahaullah adathawira ku Akka (Acre) mudziko la

Palestine pafupi ndi ndende.

Chaka cha 1868 Mirza Yahya ndiotsatira ache adapita ku Cyprus. Koma chodabwitsa

mchaka cha 1892 Bahaullah adamwalira koma Abdul Baha (Abbas Effendi) adatenga

malo udziyetsa naeso mneneri. Chaka cha 1921 Abdul Bahadaamwalira, maloache

akulowa mzukulu dzina lache ndi Shoghi Effendi naeso amwalira chaka 1957 akalibe

kubeleka kapena olowa chokoro. Koma mpakana lero lino utsogoleri uyendetsedwa ndi

guuru (Universal House of Justice).

Mirza Ghulam Ahmad anabadwa mumdzinda wa Qadiyan mudziko la India, chaka cha

1830. Adapata maphudziro ndi ma Shie ndi ma Sunni. Atatha adalowa nchito ya

ukalembera ya Comishona waku Sialkoto koma anagwa mayeso katatu kuti apezenchito

yapamwamba. Kenaka, ankafunitsitsa kuyamba zaulaliki upyolera mu studio. Iyeyo

anali kupezeka ndi mbusa Rev. Butler omwe anali mu Kristo wa Mission. Koma adapeza

mpata wina kwa Komisione wa chibili. Koma mchaka cha 1876 Ghulam Ahmad ahmad

adleka nchito ndi kubwelera ku Qadiyani pambuyo atamwalira bambo wake.

Patapita zaka zambiri , anazicha munthu ophudzira, mbusa, mphudzitsi (Bait) ochinjiliza

chipembezo kenaka kusintha malamuro monga momwe ankachitira Bab ndikuzicha

mneneri Mahdi, kenaka mneneri. Ena mwabanja lache monga mkadzi oyamba ndi adia

ana anakana kuti avomere za uneneri wake. Koma ena onse adamtsarira iyeyu ndikuzicha

iwowo ndi Aslam koma ena sanavomere zakuti iyeyu ndi mneneri ai adawacha ma

(Kafir).

Asilamu enIenI anati Ghulam Ahmad ndi ose omutsatira ndi ma Kafir si Asilamu ai,

mpakana lero Asilamu onse akukana kuti iwowo Sali Aslam ai aguulula Ghulam Ahmad.

Ghulam Ahmad andamwalira chaka cha 1908 kumatenda ya chipindupindu (cholera) ndi

kutsegura mmimba, ndipo adafa olumala, Diabetes, ndiopenga (Dementia). Patapita

dzaka zambiri. Ata mwalira Ghulam Ahmad otsatira ache adagawanika maguuru awiri

monga 1 = Qadian 2 = Lahoris.

Chimodzi modzi monga (Zorasterism, Judaism, Christianity, Chaldean, ndi Sabean

zipembezo) naoso adapita mmabvuto monga omwewa talankhula, magulu ndi midzi

ataikana ndie zosezi tanazi njira yokha yokha yobasi ndi chipembezo cha Islam, chomwe

chilindi mneneri aona, omali za Muhammad (S.A.W) Mulungu ekha ndiye omwe adzetsa

mabvuto ya (Earthquake) ndi zina zache. Koma aneneri onyenga anayamba kale

chiyambi cha Judaism.

Allama Iqbal ati: zosezi ndizo nyatsa kwabasi muchi Islam. Msokonezo mkati mwa a

Shia aku iran ndi maphudzitso awo amaononga chipembezo (Buruz Hulul, Zill).

Chimodzi modziso monga guru la sunni ugawanikana ma guru ambiri ndi ma Sufi monga

otsatira za Chilla, Kashaf, Ilham, kukhala pamodzi ndi chipembezo cha Islam. Koma

Bahai ndi Ahmadi akalipo chi*****wa cha umbuli wa Mullahism ndi thandizo uchokela ku

Britain.

Omwe Ali Asilam, onse padziko lapasi akukana kuti awa ma Qadiani ndi ma Bahai kuma

Britain akali kuwathandiza iwowo. Angakhale zitero anthuwa amango chepekela

pang’ono pang’ono mphabvu za ulaliki zikuchepekera kwa iwowo.

 

MABUUKU ENA

. Roohani Khazain by Mirza Ghulam A. Qadiani

. BAhaullah and the new era By J.E. Esselemont

. Qadianies and the Orthodox Muslims by Iqbal

. Jhootey nabi false prophets by Rafiq Dilawari

. Talbess-E-Iblees by Rafiq Dilawari

Translated in Nyanja by :

OLEMBA NDINE SHEIKH ASSADULLAH MWALE

MUFTI OF ZAMBIA

P. O. BOX FW 306

LUSAKA – ZAMBIA

CELL: +260 97 7493870

EMAIL:assadullahmwale@yahoo.com

Anti Ahmadiyya Movement in Islam

Dr Syed Rashid Ali

P.O.Box 11560 Dibba Al Fujairah

United Arab Emirates.

E-mail: rasyed@emirates.net.ae / alhafeez.org/rashid

اضيف بواسطة :   admin       رتبته (   الادارة )
التقييم: 0 /5 ( 0 صوت )

تاريخ الاضافة: 26-11-2009

الزوار: 2112


المقالات المتشابهة
المقال السابقة
Qadianis Hopes Dashed
المقالات المتشابهة
Religious Adventurism
Religious Adventurism in Islam
Religious Adventurism in Islam
المقال التالية
Where is the Grave of Jesus
جديد قسم مـقـالات الموقـــع
القائمة الرئيسية
البحث
البحث في
القائمة البريدية

اشتراك

الغاء الاشتراك